30/05/2022
Part (3) Wolemba Mark2
π‘ π‘ π‘ π‘ π‘ π‘ π‘ π‘ π‘ π‘
Musaiwale tikupitiliza nkhani yathu. mongokukuni,ma comments ani ndi ma like mdiamene amapeleka chilimbikiso kwa olembafe
Continue π
Atamaliza kuyankhula mkaziyo ndinamufunsa k*ti ndiziwe chomwe amafuna k*ti ndimuthandize koma ndinazizimuka ndimau amene anandiyankha (ayini inetu ndimakhulupila k*ti mungathe kumusamala nkazi ndipo ndikuziwa k*ti mau angawa ndikupeleka kwa munthu oyenela)
Nditanva izi ndinazizimuka koma sindinafune kumuonesela. Mwachidule ndinamuyankha k*ti eya ndizoona koma mukuziwa Joseph ndi mzanga ok*ti tachoka k*tali ndie sindingamupange chipongwe. Koma ngati mukufuna ndikhoza kuk*thandizani pa vuto lomwe mulinayo ya kumuzi. Apatu chomwe mdikatanthauza ndimati ndimubweleke ndalama k*ti atumize kwao k*ti akazayambanso ntchito azandibwezele.
Koma chomwe anandiyankha anati ok mulimonsemo ayini inu ndi mamuna ine ndi mkazi ndie palibe chomwe chingavute. Mosakhalisa ndinalowa mnyumba kukatenga ndalama kumupasa k*ti akatumizile mayi ake mamuna wake asanabwele ndipo zinathekadi.
Mazulo k*tada ndinadabwa phokoso mkaziyo akulila nditayandikila pa chiseko ndimazindikila k*ti anali akumenyedwa ndi mamuna wake. Jose! Jose! Ndinaitana uku ndikugogoda chiseko atatuluka ndinamufunsa k*ti andiuze chomwe chimachitika koma palibe chomwe analankhula chonveka chifukwa anali atalezelelatu. Izitu zinandinvesa chisoni maka ndikaganizila sogolo ya nkaziyo.
Mosataya nthawi ndinabwelela m'room yanga kukagona. Mmawa k*tacha ndinanyamuka wa kuntchito mazulo nditaweluka ndinabwelela panyumba Nditafika ndinatenga 4n yanga koma ndinadabwa k*ti ndapangidwa Hi ku WhatsApp page yanga pa number yachilendo nditayang'anisisa pc anali nkazi yemweuja. Nditamuyankha tinayamba kucheza koma ndinadabwa mmene nkaziyu akamasukila. Anandiuza k*ti ayini mumandisangalasa oti ndimaganiza k*ti popanda inu ine ndikanavutika pano ndipo ndipo mutandipepha k*ti ndikuchitileni chilichonse ndikhoza kuchita.
Chifukwa cha machezedwe athu, mwa zizizi ndinazindikila ndagwa nae m chikondi nkaziyi ndipo malonjezo anayambika koma chomwe chikavuta ndi mpata ok*ti tikumane pa awili monga muziwa anthu oyandikana.
Komatu ngakhale ndikapanga izi ndinali okhuzika maka ndikaganizila komwe ndachoka ndi nzangai. Potengela mmene tikamasukilana ndi mzangao sikulina tili ku ntchito ndinamufunsa Joseph k*ti andiuze chichikuvuta mbanja mwake k*t asamagwilizane ndi mkazi wake koma ndinatutumuka atandiyankha k*ti
Wait part 4 β‘β‘β‘β‘