05/01/2020
Moninose abale mwambuye
ngati mulibwino ndili okondwa.
ndafuna tigawane mawu ogulila moyo vuto lathu ndikunyozela ndiposo sitidziwa kuti ndizoona koma timadzitsutsa zoona ndiku tsata zosadziwa kutsogolo
kwe,
TAVANI KANKHANI AKA
Panali nkhalamba ina yakale
agogowa anakhala pa mpando, panyumba yawo anaona nkhuku komaso chiwala pabwalo lanyumbayo posa khalitsa anoona nkhuku yinja ikuthamangitsa chiwala chija
mosalekeza chiwala chikati chidumphe nkhuku ilipambuyo
zita zunglitsana kwakanthawi
chiwala chinatopa mwamwayi
chinadumpha ndiku gwela mubotolo lagilasi nkhuku yija inayesele kupisa mulomo koma
mutuwake sunakwanitsa kulowa kom itayesa ndikutopa ,
TIYENIBE
inapuma pasipa mntengo chiwalaso chitazindikila kuti chili
chotetezeka nachoso chinapuma koma kamba kakudziva kuti chapeza mphavu
chinadumpha ndikutuluka nayoso nkhuku itaona inanyamuka ndikuyambaso kuthamangitsa chiwalacho koma poti kunalibe maloena oti chiwalacho chingapulumuke
nkhuku yija inagwila chiwalacho ndiku chipha ndikuchidya.
TANTHAUZO LANTHANOYI
Agogo aja akuyimila mulengi amene amayang'anila chilengedwe chose nkhuku yija ikuyimila satana amene amatilondalonda palipase kufunakuti tisiye malamulo amulengi kuti titsate zachikunja
kuti tionongeke botolo lagilasi lija likuimila malamulo amulengi
poti ngati ulimnkati mwamalamulo amulengi umakhala otetezeka pot umakhala opulumuka kumisa mpa yadziko kudziva mphavu kuja kuyimila munthu amene amadziva kupelewela mntendele mumalamulo amulengi ndiku yambaso kutsata njila zadziko kumapeto ake umadyedwa ndi chilango ndikutsikila kumanda.
ODALA NDIWO AVETSA MAWU
WA .Ame
Palibe ofunika popanda make
zamdziko ndi zachabe chabe
tikonde malamulo amulengi.
TIDZAKHALA NDI MOYO .
Ine ganizani B N zenengeya m,balewanu mwambuye nditi mntendele ndiokoma.